The Lost Sheep--Chichewa Edition

ebook Phunziro la fanizo la Yesu Kuchokera pa Luka 15: 3-7

By F. Wayne Mac Leod

cover image of The Lost Sheep--Chichewa Edition

Sign up to save your library

With an OverDrive account, you can save your favorite libraries for at-a-glance information about availability. Find out more about OverDrive accounts.

   Not today

Find this title in Libby, the library reading app by OverDrive.

Download Libby on the App Store Download Libby on Google Play

Search for a digital library with this title

Title found at these libraries:

Library Name Distance
Loading...

NKHOSA YOTAYIKA

Phunziro la fanizo la Yesu Kuchokera pa Luka 15:3-7

Uwu ndi ndemanga pa fanizo la nkhosa yotayika monga momwe Yesu ananenera pa Luka 15:3-7. Kunena zowona, ndi vumbulutso la mtima wa Mulungu kwa iwo amene alimbana ndi chikhulupiliro chawo, agwa mu uchimo kapena adzipeza okha osayanjana ndi anthu ake.

Fanizoli silikunena zambiri za nkhosa yotayika koma za M'busa ndi zimene amachita kuti apeze nkhosa yotayikayo ndi kuibwezeretsa ku khola. Mwa M'busa ameneyu, tikuona chitsanzo champhamvu cha zimene Mulungu amafuna kwa ife monga anthu ake pamene tikuchita mogwirizana ndi nkhosa zotayika za m'tsiku lathu.

The Lost Sheep--Chichewa Edition